Adzukulu amangilira njonda ziwili pamtengo ku manda a Kabwabwa

Adzukulu okumba manda amangilira anthu awili pamtengo kumanda a Kabwabwa kamba kotolera chipepeso cha maliro popanda chilolezo kuchokera kwa amfumu a ku Area 25B (Kabwabwa) munzinda wa Lilongwe. Mayina a anthu awili omwe amangidwa pamtengowa ndi a Yusuf Steven komanso a Patrick Tambula. Nkhani yonse ikuti mderali munachitika zovuta ndipo anyamatawa anayamba kusonkhanitsa chipepeso popanda […]

The post Adzukulu amangilira njonda ziwili pamtengo ku manda a Kabwabwa appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください