Boma lawonjezera ndalama yopita kuthumba la CDF kufikapa 200 miliyoni

Kuwonjezera kwa ndalama zachitukuko za Constituency Development Fund (CDF) kuchoka pa 100 miliyoni kufika pa 200 million kwacha kunadzetsa chimwemwe chochuluka kwa aphungu ambili pamene nduna ya za chuma a Simplex Chithyola Banda anawuza nyumba ya malamulo zankhaniyi dzulo. Aphungu ena ati kukweza kwa ndalamayi kuthandiza kuti aphungu akwanilitse kutumikira anthu m’madera awo pantchito zachitukuko […]

The post Boma lawonjezera ndalama yopita kuthumba la CDF kufikapa 200 miliyoni appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください