Kamlepo wakwiya, ati ngati boma lipitilize kukondera asamukira ku Tanzania

Phungu wadera lakumvuma kwa boma la Rumphi a Kamlepo Kalua wati ndiwokonzeka kukhala nzika ya dziko la Tanzania ngati boma lipitilize kupereka ntchito za chitukuko mokondera. Polankhula mnyumba ya malamulo masanawa a Kalua ati mzodandaulitsa kuti boma likuyenera kukwanilitsa malonjezano ake pa nkhani ya chitukuko kudera lawo pofotokoza kuti kuli mavuto mavuto ambiri. Iwo ati […]

The post Kamlepo wakwiya, ati ngati boma lipitilize kukondera asamukira ku Tanzania appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください