Anjatwa kamba kopezeka ndi ngaka, nyanga za njovu

Mzibambo wa zaka 47 munzinda wa Lilongwe wathilidwa dzingwe kamba kopezeka ndi ngaka (pangolin), pomwe awiri enaso munzinda omwewu awanjata chifukwa chopezeka ndi nyanga za njovu. Izi ndi malingana ndi ofalitsa nkhani pa polisi ya Lilongwe a Hastings Chigalu omwe azindikira mzibambo opezeka ndi ngaka-yu ngati a Gevinala Makanda pomwe opezeka ndi nyanga za njovu-wa […]

The post Anjatwa kamba kopezeka ndi ngaka, nyanga za njovu appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください