Mauthenga ena abodza akuika pa chiopsezo miyoyo ya anthu omwe ali ndi HIV — yatero NAC

Bungwe la National Aids Commission (NAC) ladandaula ndi kukhudzidwa ndi mauthenga ochuluka komanso malonda okhudzana ndi machiritso a HIV ndi Edzi omwe akumafalitsidwa kwambiri. Chikalata chomwe bungweli lalemba mosogozedwa ndi mkulu wake Betreace Lydia Matanje chati mauthenga komanso malonda abodza, osayenera komanso osokoneza ndioika pa chiopsezo miyoyo ya anthu ambiri omwe ali ndi HIV. Chikalatachi […]

The post Mauthenga ena abodza akuika pa chiopsezo miyoyo ya anthu omwe ali ndi HIV — yatero NAC appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください