Mlaka asusa mphekesera zoti akudwala mwakayakaya, akuti thupi latha chifukwa chosala kudya

Mmodzi wa oyimba nyimbo zauzimu, yemwenso ndi m’busa wa mpingo wa Fountain Gates Assembly, McDonald MlakaMaliro, watsutsa mphekesera zoti iwowa akudwala mwa kayakaya. Kudzera mu program yomwe Times Radio imacheza ndi mbusayu ndi mkazi wawo Benadetta, iwo ati thupi lawo latha chifukwa cha kusala kudya osati nthenda ayi.   “Ndakhala ndikusala kuyambira chaka chatha mwezi […]

The post Mlaka asusa mphekesera zoti akudwala mwakayakaya, akuti thupi latha chifukwa chosala kudya appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください