Mfumu yaikulu ya angoni ku chigawo chakumpoto Inkosi Ya Makosi M’mbelwa Ya Chisanu yayamba yaimitsa kaye mafumu asanu kamba kothandizira kuwononga chilengwe. Mfumu Mbelwa yayankhura izi pa mwambo wobzala mitengo womwe unachitikira pa sukulu ya pulayimale ya Luwelezi m’dera la Inkosi Mabilabo. Mafumu omwe awayimitsawa ndi monga a Chihema, Kasankha, a Chiziyani, a Mchitilare komanso […]
The post Inkosi M’mbelwa yaimitsa mafumu asanu appeared first on Malawi 24.