Katswiri akuti DPP siyonkhonzeka kulowa m’boma, kwachuluka zibwana

Katswiri olankhulapo pa nkhani zosiyanasiyana m’dziko muno Latim Matenje wati zomwe zikuchitika Ku nyumba ya malamulo maka ku mbali ya aphungu otsutsa a chipani cha DPP zikuwonetseratu kuti chipanichi sichili chikonzeka kulowa m’boma. Malinga ndi Matenje, wapempha ma bwalo a milandu kuti abwere poyera ndikunena ngati atopa ndi  kumva nkhani zokhuza chipani cha DPP kusiyana […]

The post Katswiri akuti DPP siyonkhonzeka kulowa m’boma, kwachuluka zibwana appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください