Bambo amafuna kugulitsa mwana pa mtengo wa K7 miliyoni

Bambo wina ku wa zaka 24 wamangidwa ku Kasungu kamba koguna kugulitsa mwana wake pa mtengo wa K7 miliyoni. Bamboyu yemwe dzina lake ndi Noel Kanyama amafuna kugulitsa mwana wake kwa mkulu wina ochita malonda mtauni ya Kasungu. Mneneri wa apolisi ku Kasungu a Joseph Kachikho wati anayimbira foni wa malondayo kuti ali ndi mwana […]

The post Bambo amafuna kugulitsa mwana pa mtengo wa K7 miliyoni appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください