Dziko la Israel likufuna a Malawi okwana 100,000

Dziko la Israel lati likufuna a Malawi okwana 100,000 kuti akagwire ntchito zosiyanasiyana ku Israel. Izi zayankhulidwa lero pamene  nduna  ya zachuma mu dziko la  Israel,  Nir Barakt,  anali ndi mkumano ndi mlembi wamkulu mu unduwa wa zachuma mu dziko lino Dr Betchani Tchereni. A Barakt atsimikizira kuti mwai wa ntchito ulipo wambiri dziko la […]

The post Dziko la Israel likufuna a Malawi okwana 100,000 appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください