Bwalo la milandu ku Zomba layamba kumva mulandu wa a Bon Kalindo

Bwalo la Principal Resident’s Magistrate ku Zomba layamba kumva mulandu wa mkulu wa Bungwe la Malawi First a Bon Kalindo omwe akuwaganizira kuti adayambitsa chisokonezo pa ziwonetsero zomwe adachititsa mu Mzinda wa Zomba pa 23 November chaka chatha. Apolisi atsekulira mulandu a Bon Kalindo powaganizira kuti adayambitsa chisokonezo panthawi yomwe adachititsa ziwonetsero mu mwezi wa […]

The post Bwalo la milandu ku Zomba layamba kumva mulandu wa a Bon Kalindo appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください