Katelele Ching’oma watisiya

M’modzi mwa oyimba odziwika bwino ku ku Malawi, Katelele Ching’oma, watisiya. Oyimbayu wamwalira lero ku chipatala cha Kamuzu Central ku Lilongwe komwe anatengeredwa. Mchimwene wake wa oyimbayu, a Elvis Ching’oma, wati Katelele amadwala nthenda yokhudza chiwindi. Moses Makawa, yemwe anali mnzake wa Katelele wati oyimbayu anagonekwdwa ku chipatala masiku atatu apitawa. “Amadwala inde koma masiku […]

The post Katelele Ching’oma watisiya appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください