Anthu 7 apezeka ndi kachirombo ka Covid-19 ku Nsanje

Pomwe anthu ochuluka anayamba kuiwala za matenda a Covid-19, zadziwika kuti matendawa anakalipo mdziko muno pomwe ku Nsanje akuti anthu asanu ndi awiri (7), apezeka ndi kachirombo koyambitsa matendawa. Izi ndi malingana ndi a George Mbotwa omwe ndi m’modzi mwa akuluakulu ku ofesi ya zaumoyo m’boma la Nsanje omwe atsimikizira nyumba zina zofalitsa nkhani mdziko […]

The post Anthu 7 apezeka ndi kachirombo ka Covid-19 ku Nsanje appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください