Mnyamata wadzimangilira kamba kodzudzulidwa

Mnyamata wa zaka 18 zakubadwa yemwe anali mu fomu 1 wafa atadzinjatilira pa mtengo ku Mponela m’boma la Dowa kamba kakuti amadzudzulidwa pakhalidwe lake lochita  maubwezi ndi atsikana osiyanasiyana. Nkhani yonse ikuti mnyamatayu yemwe dzina lake ndi Hastings Chakufuma, amakhala ndi azakhali ake ndipo anamudzudzula kamba ka khalidwe lopanga zibwenzi ndi atsikana osiyanasiyana. Lolemba pa […]

The post Mnyamata wadzimangilira kamba kodzudzulidwa appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください