Pita koma usakachimweso: Wanderers ayiletsa kusewera mpira ku Malawi koma isewerabe

Timu ya Mighty Mukuru Wanderers yapulumukira dzenje lokumbakumba pomwe bungwe loyendetsa mpira mdziko muno la FAM lauza timuyi kuti isachimwenso kwa chaka chimodzi kuti isalandile chilango chomwe bungweli linapeleka choti Wanderers isatenge nawo gawo pa mipikisano yonse m’dziko muno kamba konyanyala masewero a chikho cha Airtel Top 8.  Pa 6 December chaka chatha, timu ya […]

The post Pita koma usakachimweso: Wanderers ayiletsa kusewera mpira ku Malawi koma isewerabe appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください