Sukulu ku Zambia zikhalabe zotseka kamba ka Cholera

Dziko la Zambia, lomwe ndi neba wa Malawi, lati sukulu m’dzikoli zikhalabe zotseka mpaka pa 29 January, 2024  kamba ka muliri wa cholera womwe wabuka dzikolo. Chikalata chomwe unduna wa za maphunziro mogwirizana ndi unduna wa za umoyo watulutsa chati sukulu zonse zaboma komaso zomwe si za boma zaimitsidwa kaye ngati njira imodzi yochepetsa kufala […]

The post Sukulu ku Zambia zikhalabe zotseka kamba ka Cholera appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください