A Malawi akusangalala kuno, palibe waombeledwa – yatelo kampani yomwe yalemba a Malawi ntchito ku Israel

Arava Farm yomwe ndi imodzi mwa kampani zomwe zatenga a Malawi kukagwira ntchito mdziko la Israel, yati anthu mdziko muno asadere nkhawa za umoyo wa azibale awowa ponena kuti anthuwa akugwira ntchito mosangala kwambiri, ndipo yatsutsa mphekesera zoti m’Malawi m’modzi waombeledwa ndi gulu la nkhondo la Hamas. Wayankhula izi ndi m’modzi mwa akuluakulu a kampani […]

The post A Malawi akusangalala kuno, palibe waombeledwa – yatelo kampani yomwe yalemba a Malawi ntchito ku Israel appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください