Apolisi ku Kasungu anjata bambo wina wazaka 29 wina yemwe akumuganizira kuti anapha mzake wazaka 28 dzana pa khilisimasi pomumenya ndi khasu m’mutu. Malingana ndi mneneri wa apolisi m’bomali a Joseph Kachikho ati bambo yemwe akumuganizira kuti adapha mzakeyu ndi a Yamikani Mlotha ndipo ophedwayu ndi a Paul Banda. Nkhani yonse ikuti awiliwa anapita ku […]
The post Wapha mzake pa khilisimasi pomumenya ndi khasu m’mutu appeared first on Malawi 24.
Moni Malawi 
