Malaulo: Mfumu yapereka pathupi kwa mwana wazaka 16

Zina ukamva ngati kumaloto ndithu. Apolisi m’boma la Kasungu amanga mfumu Mwimira yazaka 52 kamba  kogwilira mdzukulu wake wazaka 16 ndikumpatsanso pathupi. Malingana ndi mneneri wa apolisi m’bomali a Joseph Kachikho, makolo amwanayu anadabwa kumuona mwanayu akuwoneka kuti ali ndi pathupi  koma mwanayu samanena yemwe anampatsa pathupipo. Atamupanikiza ndi mafunso, mwanayu adawulula kuti pathupipo adampatsa ndi […]

The post Malaulo: Mfumu yapereka pathupi kwa mwana wazaka 16 appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください