Boma lapereka nyumba 20 kwa apolisi m’dziko muno

Apolisi ku Ndirande tsopano akhala akusimba lokoma pamene nduna ya zachitetezo a Kenneth Zikhale Ng’oma lero yatsekulira nyumba zamakono zokwana 20 zomwe boma la a  Lazarus Chakwera lamanga mgawo la nyumba 10,000 zomwe zikhale zikumangidwa m’dziko lino. Kutsatira lonjezo lomwe adachita a Chakwera mchaka cha 2020, pofika lero bomali lamangapo nyumba zokwana 1028, ndipo 20 […]

The post Boma lapereka nyumba 20 kwa apolisi m’dziko muno appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください