Zomwe achita a Msonda zaonetsa kukhwima nzeru pandale, watero katakwe pandale

M’modzi mwa akatakwe omwe amatsatira bwino pa nkhani za ndale mdziko lino a Lydford Chadza ayamikira zomwe  achita a Ken Msonda popepesa kwa mtsogoleri wa chipani  cha DPP a Peter Mutharika ndipo iwo ati izi zaonetsa kukhwima mzeru pandale. A Chadza anafotokoza kuti mpungwepungwe ndi kusamvana komwe kunabuka sikukanatengera kwina kulikonse chipanichi. Kotero iwo apempha […]

The post Zomwe achita a Msonda zaonetsa kukhwima nzeru pandale, watero katakwe pandale appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください