Zipolowe zidabuka ku Zomba apolisi ataphulitsa utsi okhetsa misozi

Chipwirikiti chidabuka dzulo madzulo kwa Chikanda, Kazembe, Mpondabwino mu mzinda wa Zomba apolisi ataphulitsa utsi okhetsa misozi pambuyo padziwonesero zomwe adatsogolera ndi mkulu wa gulu la Malawi First a Bon Kalindo. Zipolowezi zidayamba pomwe anthu ozungulira mdera la Mpondabwino adakathyola nyumba yawa polisi wina ndikubamo katundu komanso kuba mizimbe nkatikati mwa police college. Zipolowezi zidapitilira […]

The post Zipolowe zidabuka ku Zomba apolisi ataphulitsa utsi okhetsa misozi appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください