Mipando ya ‘blue’ kuno ayi – phungu wati mtundu wa mipando ku nyumba ya malamulo usinthidwe

Phungu wa chipani cha Malawi Congress Party m’dera lakumwera kwa boma la Dedza a Ishmael Onani, wabwereza kupeleka pempho lomwe a kuti anamutuma ndi anthu akudera lake loti mtundu wa mipando m’nyumba ya malamulo usinthidwe usakhaleso ‘blue’. A Onani amayankhula izi lachisanu pa 17 November pomwe aphungu anyumba ya malamulo akupitilira kuwunikira ndondomeko ya zachuma […]

The post Mipando ya ‘blue’ kuno ayi – phungu wati mtundu wa mipando ku nyumba ya malamulo usinthidwe appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください