Musatiipitsile mbiri, ife anthu aku Ntcheu sitinakutumeni – munthu wina wauza Norman Chisale

Nzika ina ya m’boma la Ntcheu yadzudzula mkulu wa chitetezo wa mtsogoleri wakale wa dziko lino Peter Mutharika, a Norman Chisale, powuza dziko kuti anthu m’bomali diokwiya pakuzuzidwa kwa nzika zake zina. Izi zikudza pomwe posachedwapa a Norman Chisale omwe amachokera m’boma la Ntcheu, anauza wayilesi ya Zodiak kuti anthu m’bbomali ndiokwiya kwambiri kamba ka […]

The post Musatiipitsile mbiri, ife anthu aku Ntcheu sitinakutumeni – munthu wina wauza Norman Chisale appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください