Ofesi ya zaumoyo yapempha anthu kuti akhale ndi zimbudzi pofuna kupewa kolera

Ofesi ya zaumoyo m’boma la Zomba yapempha mafumu kuti awonetsetsese kuti anthu awo akhale ndi zimbudzi pofuna kupewa kolera. Wofalitsa nkhani ku ofesi yadza umoyo Boma la Zomba Arnold Mndalira ndiyemwe wayankhula izi ku Zomba pa msonkhano wa atolankhani omwe adakonza pofuna kudziwitsa olemba nkhani momwe kampeni ya “Tithetse Kolera” ikuyendera  m’bomali. Mndalira adati mamfumu […]

The post Ofesi ya zaumoyo yapempha anthu kuti akhale ndi zimbudzi pofuna kupewa kolera appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください