Bambo wafela ku lumu atamwa mankhwala opereka mphamvu kwa bambo

Apolisi m’boma la Mulanje atsimikiza kuti bambo wina wa zaka pafupifupi 70 wamwalira mkati mwa ndime ku malo ena ogonako alendo pomwe anamwa mankhwala a opeleka mphamvu kwa a bambo. Watsimikiza za nkhaniyi ndi ofalitsa nkhani pa polisi ya Mulanje a Innocent Moses omwe azindikira zibamboyu ngati a Leman Walama. Moses wati bambo Walama apezeka […]

The post Bambo wafela ku lumu atamwa mankhwala opereka mphamvu kwa bambo appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください