Muuzeni Mutharika’yo aime ndimuthibule bwino – watero Nankhumwa

Ngati a Peter Mutharika amayesa kuti akadutsa moyela ku convention yawo, apa ndiye aganize kawiri. A Kondwani Nankhumwa sali mocheza ndipo ati akawaswa a Mutharika. Malinga ndi wailesi ya Zodiak, a Nankhumwa ati iwo sabwelera pambuyo ndi lingaliro lawo lofuna kutenga chipani cha DPP ndinso dziko lino mu 2025. A Nankhumwa amene ndi mtsogoleri wa […]

The post Muuzeni Mutharika’yo aime ndimuthibule bwino – watero Nankhumwa appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください