Aphungu awonetsa kukhudzika ndi umphawi msukulu za dziko lino

Aphungu anyumba yamalamulo ati ndi okhonzeka kuthana ndi umphawi wamaphunziro omwe wafika pa 87 perecenti omwe ulipo makamaka msukulu za dziko lino zomwe zikubwezeretsa maphunziro pambuyo. Izi zinanenedwa pamene bungwe lowona nkhani za maphunziro la Civil Society Education Coalition (CSEC) linali ndi nkumano ndi aphunguwa komanso mabungwe mu mzinda waLilongwe omwe amakambirana njira yamakono ya […]

The post Aphungu awonetsa kukhudzika ndi umphawi msukulu za dziko lino appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください