Bambo ndi mwana afa atadya chilazi

Anthu awili m’boma la Balaka afa atadya zomwe iwo amaganizira kuti ndi chilazi. Anthu omwe afawa ndi bambo wazaka 50 ndi mwana wake wa zaka 17. Izi zadza pamene athuwa amadya zikhawo chifukwa chanjala kamba kakuti sadakolore chimanga chokwanira.. A Wongani Nyirenda omwe ndi ndi m’neri wa chipatala chachikulu cha Machinga atsimikiza ndipo ati bambo […]

The post Bambo ndi mwana afa atadya chilazi appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください