A Tembo anali munthu wabwino osati zochotsana muchipani akupanga a Mutharika – Dausi

Olira samugwira pakamwa ndipo mneneri wakale wa chipani chotsutsa cha DPP, a Nicholas Dausi, walira mokweza pa mwambo wa maliro wa a John Tembo. Poyankhula pa bwalo la za masewero la Dedza pamene amaimilira anzawo a Kondwani Nankhumwa amene ndi mtosgoleri otsutsa mu nyumba ya malamulo, A Dausi anati a Tembo anali katakwe pa ndale. […]

The post A Tembo anali munthu wabwino osati zochotsana muchipani akupanga a Mutharika – Dausi appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください