Atupele wapepesa mavenda okhudzidwa ndi ngozi yamoto ku Zomba

Mmodzi mwa akuluakulu a chipani cha United Democratic Front UDF Atupele Muluzi wapereka thandizo la ndalama yokwana K200,000 anthu omwe anakhudzidwa ndi ngozi ya moto mu nsika waukulu wa Zomba. A Muluzi apereka thandizoli kudzera Kwa mfumu ya mzinda wa Zomba Khansala Davie Maunde yomwenso yapempha anthu ena akufuna kwabwino kuti athandize anthu omwe akhudzidwa […]

The post Atupele wapepesa mavenda okhudzidwa ndi ngozi yamoto ku Zomba appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください