Apolisi alanda zigubu ku Lilongwe

Apolisi lero alanda zigubu zoposa 100 komanso mabotolo omwe anthu amafuna kuguliramo mafuta a galimoto ku Lilongwe. Mneneri wa polisi ya Lilongwe a Hastings Chigalu ati apolisi alanda zigubuzi atayendera malo othirira mafuta a galimoto. A Chigalu ati a polisi akufuna kuthana ndi mchitidwe wogula mafutawa ndi kumakagulitsa pa mtengo wokwera. Lachiwiri sabata lino bungwe […]

The post Apolisi alanda zigubu ku Lilongwe appeared first on Malawi24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください