Bambo wafa mgodi wa golide utadilizika ku Kasungu

Bambo wa zaka 45 wafa m’mudzi wa Maluzi ku Kasungu atakwililika mu mgodi omwe amakumbamo golide. Bamboyu dzina lake ndi Godfrey Chirombo. Malingana ndineneri wa polisi ya Kasungu, Sub-Inspector Jospeh Kachikho, a Chirombo pamodzi ndi mwana wawo analowera ku mtsinje wa Chithimbiri womwe uli m’deralo kuti akafukule mwala golide Mwana wawoyo anawasiya kaye a Chirombo […]

The post Bambo wafa mgodi wa golide utadilizika ku Kasungu appeared first on Malawi24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください