Ace Jizzy, Bee Jay akana K12m kuti ayambe kuyiba nyimbo zauzimu

Oyimba nyimbo za hipapu Ace Jizzy komaso Bee Jay, akana K12 miliyoni yomwe malume awo anati awapatsa ngati awiriwa angavomere kusiya kuyimba nyimbo za chikunja ndikuyamba kuyimba nyimbo zauzimu. Malume a anyamatawa a Israel Ndelezina omwe ndi mtumiki wa Mulungu, analemba patsamba lawo la nchezo la fesibuku kufotokoza za khumbo lawo loti Ace Jizzy komaso […]

The post Ace Jizzy, Bee Jay akana K12m kuti ayambe kuyiba nyimbo zauzimu appeared first on Malawi24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください