Chakwera atuma Joyce Banda ku maliro

Mtsogoleri wakale wa dziko lino Dr Joyce Banda wanyamuka lero kupita mdziko la Kenya komwe watumidwa ndi a Lazarus Chakwera kukawaimilira pa maliro a mtsogoleri wakale wa dzikolo a Mwai Kibaki. A Kibaki omwe anali ndizaka 90, anamwalira lachinayi sabata yatha pa 21 April ndipo thupi lawo likuyembekezeka kulowa mmanda loweluka lino pa 30 April. […]

The post Chakwera atuma Joyce Banda ku maliro appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください

コメントを残す

メールアドレスが公開されることはありません。 が付いている欄は必須項目です